AYITANIDWA KWA NTHAWI YOYAMBA

 MAFAITI, KHUNGWA, WALLACE AYITANIDWA KU FLAMES

Mphunzitsi watimu ya dziko lino, Kalisto Pasuwa, wayitana 22 omwe alowe m'bindikiro kukonzekera masewero a matimu anayi ku Botswana kumathero a mwezi uno.

Mphunzitsiyu waitanako Charles Mafaiti wa Civil Service United koyamba ku m'bindikirowu monganso Alex Kambirinya, Hermas Masinja, Dan Sandukira ndi Festus Duwe.

Mpikisanowu udzayamba pa 23 March mpaka pa 31 March ndipo matimu a Botswana, Zimbabwe ndi Zambia ndi enanso omwe atenge nawo mbali.

Awa ndi osewela onse omwe ayitanidwa mu camp ya flames:

OTCHINGA PAGOLO

Dalitso Khungwa

George Chikooka

Joshua Waka

OTCHINGA KUMBUYO

MacDonald Lameck

Blessings Mpokera

Alex Kambirinya

Emmanuel Nyirenda

Fanizo Mwansambo

Hermus Masinja

Charles Mafaiti

Dan Sandukira

OSEWERA PAKATI

Yankho Singo

Moses Banda

Blessings Singini

Festus Duwe

Uchizi Vunga

Chawanangwa Gumbo

OMWETSA ZIGOLI

Andrew Joseph

Ephraim Kondowe

Allen Chihana

Wallace Adam

Gaddie Chirwa


Wolemba: Steven Pangani 

Source: Football Association of Malawi

Video: Showing Malawi National football team preparations 



Comments

Popular posts from this blog

MWAMBO UWONESEDWA PA KANEMA

ON THE WAY TO WOMEN FIFA U20

IRAN WITHDRAW FIFA WORLD CUP